Song Lyrics Search Engine

Lyrics  »  National Anthem lyrics  » 

malawi native anthem text lyrics

national anthem
Artist: national anthem
Song: malawi native anthem text
1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.
Sent by Carlos André Pereira da Silva Branco
national anthem
malawi native anthem text lyrics
by national anthem lyrics
xtc
rook lyrics
by xtc lyrics
queen
marriage of dale and ming lyrics
by queen lyrics
Latest Lyrics Additions: Hey Zeus the Dungeon / Snake In The Grass / Homies / G Check / Fuck The Club Up / Bricksquad / San Antonio Baby / Two Houses / To Me / One Less / Broken Girl / Hit the Parking Lot / Troubled World Pt.2 / Party / I Still / Everyday Struggle / Change / Can't Stay Away / The Perfect Space / I And Love And You